Wildebeest analysis examples for:   nya-nya   “Word;    February 25, 2023 at 00:56    Script wb_pprint_html.py   by Ulf Hermjakob

15474  PSA 91:14  “Chifukwa iye amandikonda,” akutero Yehova, “Ndidzamulanditsa; ndidzamuteteza pakuti wavomereza dzina langa.
24631  MRK 9:24  Nthawi yomweyo abambo a mwanayo anafuwula kuti, “Ndikhulupirira; thandizani kusakhulupirira kwanga!”
25799  LUK 18:42  Yesu anati kwa iye, “Onanso; chikhulupiriro chako chakupulumutsa.”
26768  JHN 14:31  koma kuti dziko lapansi lizindikire kuti Ine ndimakonda Atate ndi kuti ndimachita zokhazokha zimene Atate wandilamulira Ine. “Nyamukani; tizipita.”
27793  ACT 22:21  Pamenepo Ambuye anandiwuza kuti, “Nyamuka; Ine ndidzakutuma kutali kwa anthu a mitundu ina.”
28940  2CO 4:13  Kwalembedwa kuti, “Ndinakhulupirira; nʼchifukwa chake ndinayankhula.” Popeza ife tili ndi mtima womwewo wokhulupirira, ifenso timakhulupirira ndi kuyankhula,